Kupititsa patsogolo kupezeka kwa Mbewu ndi Chakudya mMalawi: Gawo lomwe Nyunda za mbewu zaku muzi ('Improving Seed and Food Security in Malawi: The Role of Community Seed Banks')

FNI Policy Brief 3/2022. Lysaker, Fridtjof Nansen Institute,  June 2022, 9 p. Translation into Chichewa of the English original.

Mfundo Zikuluzikulu:

  • Alimi ang’ono ang’ono amadalira ulimi wa mbewu zosiyanasiyana pogwiritsa ntchito mbewu zamakolo. Kasinthasintha ameneyu akuwathandizila mu nthawi yakusintha kwa nyengo komanso kupeza chakudya chofunikira mthupi lawo.
     
  • Ngakhale zili choncho mbewu za makolozo zikupitilira kusowa komanso madera ena zinatheratu.
     
  • Kasinthasintha wa mbewu kuno ku Malawi anachepa kamba kamalamulo okhuza mbeu omwe sakusimikiza kwambiri zakufunika kwa mbeu za lokolo pothandizila kuthetsa njala komaso kuthandizila popeza magulu onse achakudya.
     
  • Nyumba za mbewu za kumudzi zimathandizila kapezekedwe ka mbewu za makolo ndi kasamalidwe ka chakudya pokhala ngati likulu loyambitsanso kasinthasintha wa mbewu za makolo.
     
  • Kuonjezera nyumba za mbewu za kumudzi ndi njira imodzi yofunikira kupitisa patsogolo kupezeka kwa mbewu ndi chakudya kwa alimi ang’onoang’ono M’malawi.

Documents

FNI AUTHORS

  • Research Director, Biodiversity and Natural Resources
    +47 95118037

    Email

    randersen@fni.no
    Show Email
  • Researcher
    +47 97303118

    Email

    vmvasquez@fni.no
    Show Email

RELATED RESEARCH AREA(S)

logo_footer_fni